Yohane 14:6 - Buku Lopatulika6 Yesu ananena naye, Ine ndine njira, ndi choonadi, ndi moyo. Palibe munthu adza kwa Atate, koma mwa Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Yesu ananena naye, Ine ndine njira, ndi choonadi, ndi moyo. Palibe munthu adza kwa Atate, koma mwa Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Yesu adamuyankha kuti, “Ineyo ndine njira, ndine choona ndiponso moyo. Palibe munthu angafike kwa Atate ngati sadzera mwa Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yesu anayankha kuti, “Ine ndine njira, choonadi ndi moyo. Palibe munthu angafike kwa Atate popanda kudzera mwa Ine. Onani mutuwo |