Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 14:5 - Buku Lopatulika

5 Tomasi ananena ndi Iye, Ambuye, sitidziwa kumene munkako; tidziwa njira bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Tomasi ananena ndi Iye, Ambuye, sitidziwa kumene munkako; tidziwa njira bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Tomasi adati, “Ambuye, sitikudziŵa kumene mukupita, nanga njira yake tingaidziŵe bwanji?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye ife sitikudziwa kumene Inu mukupita, nanga tingadziwe bwanji njirayo?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 14:5
10 Mawu Ofanana  

Filipo, ndi Bartolomeo; Tomasi, ndi Mateyu wamsonkho yo; Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Tadeyo;


Ndipo Iye anawayankha nanena, Mbadwo wosakhulupirira inu, ndidzakhala ndi inu kufikira liti? Ndidzakulekererani nthawi yanji? Mudze naye kwa Ine.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, anati kwa ophunzira anzake, Tipite ifenso kuti tikafere naye pamodzi.


Ndipo kumene ndinkako Ine, mudziwa njira yake.


Lamulo langa ndi ili, kuti mukondane wina ndi mnzake, monga ndakonda inu.


Koma tsopano ndimuka kwa Iye wondituma Ine; ndipo palibe wina mwa inu andifunsa Ine, Munka kuti?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa