Yohane 14:5 - Buku Lopatulika5 Tomasi ananena ndi Iye, Ambuye, sitidziwa kumene munkako; tidziwa njira bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Tomasi ananena ndi Iye, Ambuye, sitidziwa kumene munkako; tidziwa njira bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tomasi adati, “Ambuye, sitikudziŵa kumene mukupita, nanga njira yake tingaidziŵe bwanji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye ife sitikudziwa kumene Inu mukupita, nanga tingadziwe bwanji njirayo?” Onani mutuwo |