Yohane 13:32 - Buku Lopatulika32 ndipo Mulungu adzamlemekeza Iye mwa Iye yekha, adzamlemekeza Iye tsopano apa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 ndipo Mulungu adzamlemekeza Iye mwa Iye yekha, adzamlemekeza Iye tsopano apa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Ngati Mulungu walemekezedwa mwa Iyeyu, Mulungu Mwini nayenso adzamlemekeza Iye, ndipo achita zimenezi tsopano apa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ngati Mulungu walemekezedwa mwa Iye, Mulungu mwini adzalemekezanso Mwana, ndipo amulemekeza nthawi yomweyo. Onani mutuwo |