Yohane 13:31 - Buku Lopatulika31 Tsono m'mene adatuluka, Yesu ananena, Tsopano walemekezeka Mwana wa Munthu, ndipo Mulungu walemekezedwa mwa Iye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Tsono m'mene adatuluka, Yesu ananena, Tsopano walemekezeka Mwana wa Munthu, ndipo Mulungu walemekezedwa mwa Iye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Yudasi atatuluka, Yesu adati, “Tsopano Mwana wa Munthu walemekezedwa, ndipo mwa Iyeyu Mulungu walemekezedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Yudasi atatuluka, Yesu anati, “Tsopano Mwana wa Munthu walemekezedwa, ndipo mwa Iyeyu Mulungu walemekezedwanso. Onani mutuwo |