Yohane 13:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo pambuyo pake pa nthongoyo, Satana analowa mwa iyeyu. Pamenepo Yesu ananena naye, Chimene uchita, chita msanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo pambuyo pake pa nthongoyo, Satana analowa mwa iyeyu. Pamenepo Yesu ananena naye, Chimene uchita, chita msanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Yudasi atangolandira mkatewo, Satana adaloŵa mwa iye. Yesu adamuuza kuti, “Zimene ufuna kuchita, kachite mwamsanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nthawi yomweyo Yudasi atangodya bulediyo, Satana analowa mwa Iye. Yesu anamuwuza Iye kuti, “Chomwe ukufuna kuchita, chita msanga.” Onani mutuwo |