Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 13:28 - Buku Lopatulika

28 Koma palibe mmodzi wa iwo akuseamako anadziwa chimene anafuna, poti atere naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Koma palibe mmodzi wa iwo akuseamako anadziwa chimene anafuna, poti atere naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Koma mwa amene ankadyawo panalibe ndi mmodzi yemwe amene adaamvetsa zimene adaamuuzazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Koma panalibe ndi mmodzi yemwe pa chakudyapo amene anamvetsa chifukwa chimene Yesu ananenera izi kwa iye.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 13:28
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pambuyo pake pa nthongoyo, Satana analowa mwa iyeyu. Pamenepo Yesu ananena naye, Chimene uchita, chita msanga.


Pakuti popeza Yudasi anali nalo thumba, ena analikuyesa kuti Yesu ananena kwa iye, Gula zimene zitisowa pachikondwerero; kapena, kuti apatse kanthu kwa aumphawi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa