Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 13:12 - Buku Lopatulika

12 Pamenepo, atatha Iye kusambitsa mapazi ao, ndi kutenga malaya ake, anaseamanso, nati kwa iwo, Nanga chimene ndakuchitirani inu, muchizindikira kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Pamenepo, atatha Iye kusambitsa mapazi ao, ndi kutenga malaya ake, anaseamanso, nati kwa iwo, Nanga chimene ndakuchitirani inu, muchizindikira kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Yesu atatsuka mapazi a ophunzira ake, adavalanso mwinjiro wake nakakhalanso podyera paja. Kenaka adaŵafunsa kuti, “Kodi mwazimvetsa zimene ndakuchitiranizi?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iye atamaliza kusambitsa mapazi awo anavala zovala zake ndi kubwerera pamalo pake. Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukuzindikira zimene ndakuchitirani inu?

Onani mutuwo Koperani




Yohane 13:12
7 Mawu Ofanana  

Nanena nane anthu, Simudzatiuza kodi zitani nafe izi muzichita?


Momwemo Ezekiele adzakhala kwa inu chizindikiro; umo monse anachitira iye mudzachita ndinu; chikadza ichi mudzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.


Mwamvetsa zonsezi kodi? Iwo anati kwa Iye, Inde.


Ndipo ananena nao, Simudziwa kodi fanizo ili? Mukazindikira bwanji mafanizo onse?


Pakuti wamkulu ndani, iye wakuseama pachakudya kapena wakutumikirapo? Si ndiye wakuseama pachakudya kodi? Koma Ine ndili pakati pa inu monga ngati wotumikira.


ananyamuka pamgonero, navula malaya ake; ndipo m'mene adatenga chopukutira, anadzimanga m'chuuno.


Yesu anayankha nati kwa iye, Chimene ndichita Ine suchidziwa tsopano; koma udzadziwa m'tsogolo mwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa