Yohane 12:40 - Buku Lopatulika40 Wadetsa maso ao, naumitsa mtima wao; kuti angaone ndi maso, angazindikire ndi mtima, nangatembenuke, ndipo ndingawachiritse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Wadetsa maso ao, naumitsa mtima wao; kuti angaone ndi maso, angazindikire ndi mtima, nangatembenuke, ndipo ndingawachiritse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 “Mulungu adadetsa maso ao, ndipo adabunthitsa nzeru zao, kuti maso ao asaone, nzeru zao zisamvetse, kuti angatembenuke mtima, ndipo Ine ndingaŵachiritse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 “Iye wachititsa khungu maso awo ndi kuwumitsa mitima yawo, kotero kuti iwo sangathe kuona ndi maso awo, kapena kuzindikira ndi mitima yawo, kapena kutembenuka kuti Ine ndikanawachiza.” Onani mutuwo |