Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 12:39 - Buku Lopatulika

39 Chifukwa cha ichi sanathe kukhulupirira, pakuti Yesaya anatinso,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Chifukwa cha ichi sanathe kukhulupirira, pakuti Yesaya anatinso,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Iwo sadathe kukhulupirira, chifukwa paja Yesaya yemweyo adaanenanso kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Pa chifukwa cha ichi iwo sanakhulupirire, chifukwa Yesaya ananenanso kuti:

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:39
8 Mawu Ofanana  

Koma ngati ndichita, mungakhale simukhulupirira Ine, khulupirirani ntchitozo; kuti mukadziwe ndi kuzindikira kuti Atate ali mwa Ine, ndi Ine mwa Atate.


kuti mau a Yesaya mneneri akakwaniridwe, amene anati, Ambuye, wakhulupirira ndani kulalikira kwathu? Ndipo mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa kwa yani?


Wadetsa maso ao, naumitsa mtima wao; kuti angaone ndi maso, angazindikire ndi mtima, nangatembenuke, ndipo ndingawachiritse.


Mungathe inu bwanji kukhulupirira, popeza mulandira ulemu wina kwa mnzake ndipo ulemu wakuchokera kwa Mulungu yekha simuufuna?


Kulibe mmodzi akhoza kudza kwa Ine koma ngati Atate wondituma Ine amkoka iye; ndipo Ine ndidzamuukitsa iye tsiku lomaliza.


okhala nao maso odzala ndi chigololo, osakhoza kuleka uchimo, kunyengerera iwo a moyo wosakhazikika; okhala nao mtima wozolowera kusirira; ana a temberero;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa