Yohane 12:30 - Buku Lopatulika30 Yesu anayankha nati, Mau awa sanafike chifukwa cha Ine, koma cha inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Yesu anayankha nati, Mau awa sanafika chifukwa cha Ine, koma cha inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Yesu adaŵauza kuti, “Mauŵa amveka osati chifukwa cha Ine ai, koma chifukwa cha inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Yesu anati, “Mawu awa abwera chifukwa cha inu osati chifukwa cha Ine. Onani mutuwo |