Yohane 12:31 - Buku Lopatulika31 Tsopano pali kuweruza kwa dziko ili lapansi; mkulu wa dziko ili lapansi adzatayidwa kunja tsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Tsopano pali kuweruza kwa dziko ili lapansi; mkulu wa dziko ili lapansi adzatayidwa kunja tsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Tsopano ndiyo nthaŵi yoti anthu a dziko lino lapansi aweruzidwe. Tsopano Satana, mfumu ya anthu ochimwa a dziko lino lapansi, adzaponyedwa kunja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ino tsopano ndi nthawi yachiweruzo pa dziko lapansi; tsopano olamulira wa dziko lapansi adzathamangitsidwa. Onani mutuwo |