Yohane 12:29 - Buku Lopatulika29 Chifukwa chake khamu la anthu akuimirirako, ndi kuwamva ananena kuti kwagunda. Ena ananena, Mngelo walankhula ndi Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Chifukwa chake khamu la anthu akuimirirako, ndi kuwamva ananena kuti kwagunda. Ena ananena, Mngelo walankhula ndi Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Panali khamu la anthu pamenepo. Tsono pamene adamva mauwo, adati, “Kwagunda bingu.” Koma ena adati, “Mngelo walankhula naye.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Gulu la anthu lomwe linali pamenepo litamva linati, “Kwagunda bingu,” ena anati, “Mngelo wayankhula kwa Iye.” Onani mutuwo |