Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 12:22 - Buku Lopatulika

22 Filipo anadza nanena kwa Andrea; nadza Andrea ndi Filipo, nanena ndi Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Filipo anadza nanena kwa Andrea; nadza Andrea ndi Filipo, nanena ndi Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Filipo adakauza Andrea, ndipo Andrea pamodzi ndi Filipoyo adakauza Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Filipo anapita kukawuza Andreya; Andreya ndi Filipo pamodzi anakawuza Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:22
7 Mawu Ofanana  

Awa amene, khumi ndi awiriwa, Yesu anawatumiza, nawalangiza ndi kuti, Musapite kunjira ya kwa anthu akunja, ndi m'mudzi wa Asamariya musamalowamo:


Koma Filipo anali wa ku Betsaida, mzinda wa Andrea ndi Petro.


Koma Yesu anayankha iwo, nati, Yafika nthawi, kuti Mwana wa Munthu alemekezedwe.


Mmodzi wa ophunzira ake, Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, ananena ndi Iye,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa