Yohane 12:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo iwo anadza kwa Filipo wa ku Betsaida wa mu Galileya, namfunsa iye, ndi kuti, Mbuye, tifuna kuona Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo iwo anadza kwa Filipo wa ku Betsaida wa m'Galileya, namfunsa iye, ndi kuti, Mbuye, tifuna kuona Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Iwowo adapita kwa Filipo, amene kwao kunali ku Betsaida wa ku Galileya, nakampempha kuti, “Pepani bambo, timati tidzaone Yesu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Iwo anabwera kwa Filipo, wochokera ku Betisaida wa ku Galileya, ndi pempho, nati, “Akulu, ife tikufuna kuona Yesu.” Onani mutuwo |