Yohane 12:20 - Buku Lopatulika20 Koma panali Agriki ena mwa iwo akukwera kunka kukalambira pachikondwerero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma panali Agriki ena mwa iwo akukwera kunka kukalambira pachikondwerero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma panali Agriki ena pakati pa anthu amene adaakapembedza pa chikondwererocho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tsopano panali Agriki ena pakati pa amene anapita kukapembedza ku phwando. Onani mutuwo |