Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 12:11 - Buku Lopatulika

11 pakuti ambiri a Ayuda anachoka chifukwa cha iye, nakhulupirira Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 pakuti ambiri a Ayuda anachoka chifukwa cha iye, nakhulupirira Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 pakuti chifukwa cha iyeyo anthu ambiri ankaŵachokera nkumakhulupirira Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 pakuti chifukwa cha iye Ayuda ambiri amapita kwa Yesu ndi kumukhulupirira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:11
10 Mawu Ofanana  

Koma ndadziwa Ine kuti mumandimva Ine nthawi zonse; koma chifukwa cha khamu la anthu alikuimirira pozungulira ndinanena ichi, kuti akhulupirire kuti Inu munandituma Ine.


Chifukwa chake ambiri a mwa Ayuda amene anadza kwa Maria, m'mene anaona chimene anachita, anakhulupirira Iye.


Ngati timleka Iye kotero, onse adzakhulupirira Iye; ndipo adzadza Aroma nadzachotsa malo athu ndi mtundu wathu.


Koma ansembe aakulu anapangana kuti akaphe Lazaronso;


Chifukwa cha ichinso khamulo linadza kudzakomana ndi Iye, chifukwa anamva kuti Iye adachita chizindikiro ichi.


Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge,


Koma ambiri a m'khamu la anthu anakhulupirira Iye; ndipo ananena, Pamene Khristu akadza kodi adzachita zizindikiro zambiri zoposa zimene adazichita ameneyo?


Koma Ayuda, pakuona makamu a anthu, anadukidwa, natsutsana nazo zolankhulidwa ndi Paulo, nachita mwano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa