Yohane 12:12 - Buku Lopatulika12 M'mawa mwake khamu lalikulu la anthu amene adadza kuchikondwerero, pakumva kuti Yesu alinkudza ku Yerusalemu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 M'mawa mwake khamu lalikulu la anthu amene adadza kuchikondwerero, pakumva kuti Yesu alinkudza ku Yerusalemu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 M'maŵa mwake anthu ambirimbiri amene anali atabwera ku chikondwerero cha Paska chija, adamva kuti Yesu akubwera ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsiku lotsatira, gulu lalikulu la anthu lomwe linabwera kuphwando linamva kuti Yesu anali mʼnjira kupita ku Yerusalemu. Onani mutuwo |