Yohane 11:47 - Buku Lopatulika47 Pamenepo ansembe aakulu ndi Afarisi anasonkhanitsa akulu, nanena, Titani ife? Chifukwa munthu uyu achita zizindikiro zambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Pamenepo ansembe aakulu ndi Afarisi anasonkhanitsa akulu, nanena, Titani ife? Chifukwa munthu uyu achita zizindikiro zambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Apo akulu a ansembe ndi Afarisi adaitanitsa Bungwe Lalikulu la Ayuda, nafunsana kuti, “Titani pamenepa, popeza kuti munthuyu akuchita zozizwitsa zambiri? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Kenaka akulu a ansembe ndi Afarisi anayitanitsa msonkhano wa akulu olamulira. Iwo anafunsa kuti, “Kodi ife tikuchita chiyani? Pano pali munthu uyu akuchita zizindikiro zodabwitsa zambiri. Onani mutuwo |