Yohane 11:46 - Buku Lopatulika46 Koma ena a mwa iwo anamuka kwa Afarisi, nawauza zimene Yesu adazichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Koma ena a mwa iwo anamuka kwa Afarisi, nawauza zimene Yesu adazichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Koma ena adapita kwa Afarisi, nakaŵasimbira zimene Yesu adaachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Koma ena a iwo anapita kwa Afarisi ndi kukawawuza zimene Yesu anachita. Onani mutuwo |