Yohane 11:40 - Buku Lopatulika40 Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Yesu adamufunsa kuti, “Kodi sindidakuuze kuti ukakhulupirira uwona ulemerero wa Mulungu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Kenaka Yesu anati, “Kodi Ine sindinakuwuze kuti ngati iwe ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?” Onani mutuwo |