Yohane 11:41 - Buku Lopatulika41 Pomwepo anachotsa mwala. Koma Yesu anakweza maso ake kupenya kumwamba nati, Atate, ndiyamika Inu kuti munamva Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Pomwepo anachotsa mwala. Koma Yesu anakweza maso ake kupenya kumwamba nati, Atate, ndiyamika Inu kuti munamva Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Tsono anthu adachotsa chimwala chija. Yesu adayang'ana kumwamba nati, “Atate, ndikukuyamikani kuti mwandimvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Choncho iwo anachotsa mwalawo. Kenaka Yesu anayangʼana kumwamba ndikuti, “Atate, Ine ndikukuthokozani chifukwa mumandimvera. Onani mutuwo |