Yohane 11:34 - Buku Lopatulika34 nati, Mwamuika iye kuti? Ananena ndi Iye, Ambuye, tiyeni mukaone. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 nati, Mwamuika iye kuti? Ananena ndi Iye, Ambuye, tiyeni mukaone. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Tsono adaŵafunsa kuti, “Mudamuika kuti?” Iwo adati, “Ambuye, tiyeni mukaone.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iye anafunsa kuti, “Kodi mwamuyika kuti?” Iwo anayankha kuti, “Ambuye tiyeni mukaone.” Onani mutuwo |