Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:34 - Buku Lopatulika

34 nati, Mwamuika iye kuti? Ananena ndi Iye, Ambuye, tiyeni mukaone.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 nati, Mwamuika iye kuti? Ananena ndi Iye, Ambuye, tiyeni mukaone.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Tsono adaŵafunsa kuti, “Mudamuika kuti?” Iwo adati, “Ambuye, tiyeni mukaone.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Iye anafunsa kuti, “Kodi mwamuyika kuti?” Iwo anayankha kuti, “Ambuye tiyeni mukaone.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:34
7 Mawu Ofanana  

Iye mulibe muno iai; pakuti anauka, monga ananena. Idzani muno mudzaone malo m'mene anagonamo Ambuye.


Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo.


Ndipo iye ananena nao, Musadabwe: mulikufuna Yesu Mnazarene amene anapachikidwa; anauka; sali pano; taonani, mbuto m'mene anaikamo Iye!


Nanena nao, Tiyeni, mukaone. Pamenepo anadza naona kumene anakhala; nakhala ndi Iye tsiku lomwelo; panali monga ora lakhumi.


Pamenepo Yesu, pakumuona iye alikulira, ndi Ayuda akumperekeza iye alikulira, anadzuma mumzimu, navutika mwini,


Pomwepo anathamanga nadza kwa Simoni Petro ndi kwa wophunzira wina amene Yesu anamkonda, nanena nao, Anachotsa Ambuye kumanda, ndipo sitidziwa kumene anamuika Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa