Yohane 11:33 - Buku Lopatulika33 Pamenepo Yesu, pakumuona iye alikulira, ndi Ayuda akumperekeza iye alikulira, anadzuma mumzimu, navutika mwini, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Pamenepo Yesu, pakumuona iye alikulira, ndi Ayuda akumperekeza iye alikulira, anadzuma mumzimu, navutika mwini, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Yesu ataona Maria akulira, ndiponso anthu amene adaadza naye iwonso akulira, zidamkhudza kwambiri ndipo adavutika mu mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Yesu ataona iye akulira, ndi Ayuda amene anabwera naye akuliranso, anakhudzidwa kwambiri ndi kuvutika mu mzimu. Onani mutuwo |