Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:29 - Buku Lopatulika

29 Koma iyeyo, pakumva, ananyamuka msanga, nadza kwa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Koma iyeyo, pakumva, ananyamuka msanga, nadza kwa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Maria atamva zimenezi, adanyamuka msangamsanga, nadza kwa Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Mariya atamva izi, anayimirira mofulumira napita kwa Iye.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:29
7 Mawu Ofanana  

Pamene munati, Funani nkhope yanga; mtima wanga unati kwa Inu. Nkhope yanu, Yehova, ndidzaifuna.


Munthu akondwera ndi mayankhidwe a m'kamwa mwake; ndi mau a pa nthawi yake kodi sali abwino?


Chitsulo chinola chitsulo; chomwecho munthu anola nkhope ya mnzake.


Ndipo m'mene anati ichi anachoka naitana Maria mbale wake m'tseri, ndi kuti, Wafika Mphunzitsi, akuitana iwe.


(Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye.)


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa