Yohane 11:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo m'mene anati ichi anachoka naitana Maria mbale wake m'tseri, ndi kuti, Wafika Mphunzitsi, akuitana iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo m'mene anati ichi anachoka naitana Maria mbale wake m'tseri, ndi kuti, Wafika Mphunzitsi, akuitana iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Marita atanena zimenezi, adaitanira paseri Maria mng'ono wake namuuza kuti, “Afika Aphunzitsi, akukuitana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Ndipo iye atanena izi anabwerera ndi kukayitana mchemwali wake Mariya namuyankhula monongʼona pambali, nati, “Aphunzitsi abwera ndipo akukuyitana.” Onani mutuwo |