Yohane 11:30 - Buku Lopatulika30 (Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye.) Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 (Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye.) Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Pamenepo nkuti Yesu asanafike kumudziko, koma anali chikhalire pamalo pomwe Marita adaakumana naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Tsopano nʼkuti Yesu asanalowe mʼmudzi, koma anali akanali pa malo pamene Marita anakumana naye. Onani mutuwo |