Yohane 11:22 - Buku Lopatulika22 Koma ngakhale tsopano ndidziwa kuti zinthu zilizonse mukapempha Mulungu, adzakupatsani Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma ngakhale tsopano ndidziwa kuti zinthu zilizonse mukapempha Mulungu, adzakupatsani Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma ngakhale tsopano, ndikudziŵa kuti Mulungu adzakupatsani zilizonse mungampemphe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma ine ndikudziwa kuti ngakhale tsopano Mulungu adzakupatsani chilichonse chimene mudzamupempha.” Onani mutuwo |