Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:22 - Buku Lopatulika

22 Koma ngakhale tsopano ndidziwa kuti zinthu zilizonse mukapempha Mulungu, adzakupatsani Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Koma ngakhale tsopano ndidziwa kuti zinthu zilizonse mukapempha Mulungu, adzakupatsani Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Koma ngakhale tsopano, ndikudziŵa kuti Mulungu adzakupatsani zilizonse mungampemphe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Koma ine ndikudziwa kuti ngakhale tsopano Mulungu adzakupatsani chilichonse chimene mudzamupempha.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:22
10 Mawu Ofanana  

Undifunse, ndipo ndidzakupatsa amitundu akhale cholowa chako, ndi malekezero a dziko lapansi akhale akoako.


Ndipo Yesu anadza nalankhula nao, nanena, Mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine Kumwamba ndi padziko lapansi.


Ndipo Yesu ananena naye, Ngati mukhoza! Zinthu zonse zitheka ndi iye wakukhulupirira.


Yesu ananena naye, Mlongo wako adzauka.


monga mwampatsa Iye ulamuliro pa thupi lililonse, kuti onse amene mwampatsa Iye, awapatse iwo moyo wosatha.


Atate akonda Mwana, nampatsa zinthu zonse m'dzanja lake.


Tidziwa kuti Mulungu samvera ochimwa. Koma ngati munthu aliyense akhala wopembedza Mulungu nachita chifuniro chake, amvera ameneyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa