Yohane 11:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Marita anati kwa Yesu, Ambuye, mukadakhala kuno mlongo wanga sakadafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Marita anati kwa Yesu, Ambuye, mukadakhala kuno mlongo wanga sakadafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Tsono Marita adauza Yesu kuti, “Ambuye, mukadakhala kuno, sibwenzi mlongo wanga atamwalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Marita anati kwa Yesu, “Ambuye, mukanakhala muli kuno, mlongo wanga sakanamwalira. Onani mutuwo |