Yohane 11:20 - Buku Lopatulika20 Pamenepo Marita, pakumva kuti Yesu alinkudza, anamuka kukakomana ndi Iye; koma Maria anakhalabe m'nyumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pamenepo Marita, pakumva kuti Yesu alinkudza, anamuka kukakomana ndi Iye; koma Maria anakhalabe m'nyumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pamene Marita adamva kuti Yesu akubwera, adapita kukamchingamira. Koma Maria adaatsalira m'nyumba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Pamene Marita anamva kuti Yesu akubwera, anapita kukakumana naye. Koma Mariya anatsala ku nyumba. Onani mutuwo |