Yohane 11:19 - Buku Lopatulika19 koma ambiri a mwa Ayuda adadza kwa Marita ndi Maria, kudzawatonthoza mtima pa mlongo wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 koma ambiri a mwa Ayuda adadza kwa Marita ndi Maria, kudzawatonthoza mtima pa mlongo wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Panali anthu ambiri amene adaabwera kwa Marita ndi Maria kudzaŵapepesa chifukwa cha imfa ya mlongo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 ndipo Ayuda ambiri anabwera kwa Marita ndi Mariya kudzawatonthoza pa imfa ya mʼbale wawo. Onani mutuwo |