Yohane 11:18 - Buku Lopatulika18 Koma Betaniya anali pafupi pa Yerusalemu, nthawi yake yonga ya mastadiya khumi ndi asanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma Betaniya anali pafupi pa Yerusalemu, nthawi yake yonga ya mastadiya khumi ndi asanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ku Betaniya kunali kufupi ndi ku Yerusalemu, mtunda wokwanira pafupi makilomita atatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mudzi wa Betaniya unali pafupi ndi Yerusalemu pa mtunda wosachepera makilomita atatu, Onani mutuwo |