Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo pamene Yesu anadza, anapeza kuti pamenepo atakhala m'manda masiku anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo pamene Yesu anadza, anapeza kuti pamenepo atakhala m'manda masiku anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pamene Yesu adafika ku Betaniya, adapeza Lazaro atagona m'manda masiku anai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Yesu atafika, anapeza kuti Lazaro anali atagona mʼmanda masiku anayi.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:17
5 Mawu Ofanana  

Atapita masiku awiri adzatitsitsimutsa, tsiku lachitatu adzatiutsa; ndipo tidzakhala ndi moyo pamaso pake.


Ndipo kubadwa kwake kwa Yesu Khristu kunali kotere: Amai wake Maria anapalidwa ubwenzi ndi Yosefe, koma asanakomane iwowo, anapezedwa iye ali ndi pakati mwa Mzimu Woyera.


Yesu ananena, Chotsani mwala. Marita, mlongo wake wa womwalirayo, ananena ndi Iye, Ambuye, adayamba kununkha: pakuti wagona masiku anai.


Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa