Yohane 11:16 - Buku Lopatulika16 Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, anati kwa ophunzira anzake, Tipite ifenso kuti tikafere naye pamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, anati kwa ophunzira anzake, Tipite ifenso kuti tikafere naye pamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, adauza ophunzira anzake kuti, “Tiyeni ifenso tipite nao kuti tikafe naye pamodzi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, anati kwa ophunzira anzake, “Tiyeni nafenso tipite, kuti tikafere naye pamodzi.” Onani mutuwo |