Yohane 11:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ndikondwera chifukwa cha inu kuti kunalibe Ine komweko, chakuti mukakhulupirire; koma tiyeni, tipite kwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ndikondwera chifukwa cha inu kuti kunalibe Ine komweko, chakuti mukakhulupirire; koma tiyeni, tipite kwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 komabe chifukwa cha inu ndikukondwera kuti Ine kunalibe kumeneko, kuti choncho mukakhulupirire. Tiyeni tipiteko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ine ndikukondwera chifukwa cha inu kuti kunalibe kumeneko; koma kuti mukakhulupirire tiyeni tipiteko.” Onani mutuwo |