Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:12 - Buku Lopatulika

12 Chifukwa chake ophunzira ake anati kwa Iye, Ambuye, ngati ali m'tulo adzachira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Chifukwa chake ophunzira ake anati kwa Iye, Ambuye, ngati ali m'tulo adzachira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Apo ophunzira ake adati, “Ambuye, ngati wagona tulo, achira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ophunzira ake anayankha kuti, “Ambuye, ngati wagona adzapeza bwino.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:12
3 Mawu Ofanana  

ananena, Tulukani, pakuti kabuthuko sikanafe koma kali m'tulo. Ndipo anamseka Iye pwepwete.


Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take.


Koma Yesu adanena za imfa yake; koma iwowa anayesa kuti ananena za mpumulo wa tulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa