Yohane 11:11 - Buku Lopatulika11 Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Atatero adaŵauza kuti, “Lazaro, bwenzi lathu, wagona tulo, koma ndipita kuti ndikamdzutse ku tulo taketo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye atatha kunena izi, anapitirira kuwawuza iwo kuti, “Bwenzi lathu Lazaro wagona tulo; koma Ine ndikupita kumeneko kukamudzutsa.” Onani mutuwo |