Yohane 11:10 - Buku Lopatulika10 Koma ngati munthu ayenda usiku, akhumudwa, chifukwa mulibe kuunika mwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Koma ngati munthu ayenda usiku, akhumudwa, chifukwa mulibe kuunika mwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma akayenda usiku, amakhumudwa chifukwa kuŵalako alibe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma amene akuyenda usiku amapunthwa, chifukwa kuwalako alibe.” Onani mutuwo |