Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:10 - Buku Lopatulika

10 Koma ngati munthu ayenda usiku, akhumudwa, chifukwa mulibe kuunika mwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Koma ngati munthu ayenda usiku, akhumudwa, chifukwa mulibe kuunika mwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Koma akayenda usiku, amakhumudwa chifukwa kuŵalako alibe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Koma amene akuyenda usiku amapunthwa, chifukwa kuwalako alibe.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:10
9 Mawu Ofanana  

Pondifika ine ochita zoipa kudzadya mnofu wanga, inde akundisautsa ndi adani anga, anakhumudwa iwo nagwa.


Wanzeru maso ake ali m'mutu wake, koma chitsiru chiyenda mumdima; ndipo nanenso ndinazindikira kuti chomwe chiwagwera onsewo ndi chimodzi.


Lemekezani Yehova Mulungu wanu, kusanade, mapazi anu asanaphunthwe pa mapiri achizirezire; nimusanayembekeze kuunika, Iye asanasandutse kuunikaku mthunzi wa imfa, ndi kukuyesa mdima wa bii.


Koma Yehova ali ndi ine ngati wamphamvu ndi woopsa; chifukwa chake ondisautsa adzaphunthwa, sadzandilala; adzakhala ndi manyazi ambiri, chifukwa sanachite chanzeru, ngakhale ndi kunyazitsa kwamuyaya kumene sikudzaiwalika.


ndipo alibe mizu mwa iye, koma akhala nthawi yaing'ono; ndipo pakudza nsautso kapena zunzo chifukwa cha mau, iye akhumudwa pomwepo.


Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take.


Yesu anayankha, Kodi sikuli maora khumi ndi awiri usana? Ngati munthu ayenda usana sakhumudwa, chifukwa apenya kuunika kwa dziko lino lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa