Yohane 10:7 - Buku Lopatulika7 Chifukwa chake Yesu ananenanso nao, Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Ine ndine khomo la nkhosa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chifukwa chake Yesu ananenanso nao, Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Ine ndine khomo la nkhosa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono Yesu adatinso, “Ndithu ndikunenetsa kuti Ine ndine khomo la nkhosa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho Yesu anatinso, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Ine ndine khomo la nkhosa. Onani mutuwo |