Yohane 10:5 - Buku Lopatulika5 Koma mlendo sizidzamtsata, koma zidzamthawa; chifukwa sizidziwa mau a alendo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma mlendo sizidzamtsata, koma zidzamthawa; chifukwa sizidziwa mau a alendo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mlendo sizidzamtsatira ai, zidzamthaŵa, chifukwa sizidziŵa mau a alendo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma nkhosazo sizidzatsatira mlendo. Izo zidzamuthawa chifukwa sizizindikira mawu a mlendo.” Onani mutuwo |