Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 10:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo Yesu analikuyendayenda mu Kachisi m'khonde la Solomoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo Yesu analikuyendayenda m'Kachisi m'khonde la Solomoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Yesu ankangodziyendera m'Nyumba ya Mulungu, m'khonde lotchedwa Khonde la Solomoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 ndipo Yesu ankayenda mʼbwalo la Nyumbayo ku malo a Solomoni.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 10:23
3 Mawu Ofanana  

Koma kunali phwando la kukonzetsanso mu Yerusalemu; nyengoyo ndi yachisanu.


Koma m'mene anagwira Petro ndi Yohane, anawathamangira pamodzi anthu onse kukhonde lotchedwa la Solomoni, alikudabwa ndithu.


Ndipo mwa manja a atumwi zizindikiro ndi zozizwa zambiri zinachitidwa pa anthu; ndipo anali onse ndi mtima umodzi m'khonde la Solomoni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa