Yohane 10:22 - Buku Lopatulika22 Koma kunali phwando la kukonzetsanso mu Yerusalemu; nyengoyo ndi yachisanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma kunali phwando la kukonzetsanso m'Yerusalemu; nyengoyo ndi yachisanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ku Yerusalemu kunali chikondwerero chokumbukira kuperekedwanso kwa Nyumba ya Mulungu. Inali nyengo yozizira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ku Yerusalemu kunali chikondwerero chokumbukira kupatulidwa kwa Nyumba ya Mulungu. Inali nthawi yozizira, Onani mutuwo |