Yohane 10:20 - Buku Lopatulika20 Koma ambiri mwa iwo ananena, Ali ndi chiwanda, nachita misala; mukumva Iye bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma ambiri mwa iwo ananena, Ali ndi chiwanda, nachita misala; mukumva Iye bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ambiri mwa iwo ankati, “Ali ndi mizimu yoipa, ndipo wapenga. Bwanji mukumumveranso Iyeyu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ambiri a iwo anati, “Iye ndi wogwidwa ndi ziwanda ndi wamisala. Chifukwa chiyani mukumvera Iye?” Onani mutuwo |