Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 10:19 - Buku Lopatulika

19 Panakhalanso kutsutsana pakati pa Ayuda chifukwa cha mau awa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Panakhalanso kutsutsana pakati pa Ayuda chifukwa cha mau awa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Anthu adaayambanso kutsutsana okhaokha chifukwa cha mau ameneŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Pa mawu awa Ayuda anagawikananso.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 10:19
9 Mawu Ofanana  

Pamenepo Ayuda anatetana wina ndi mnzake ndi kunena, Akhoza bwanji ameneyu kutipatsa ife kudya thupi lake?


Ena pamenepo mwa Afarisi ananena, Munthu uyu sachokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata. Koma ena ananena, Munthu ali wochimwa akhoza bwanji kuchita zizindikiro zotere? Ndipo panali kutsutsana mwa iwo.


Ndipo khamu la mzindawo linagawikana; ena anali ndi Ayuda, koma ena anali ndi atumwi.


Pakutitu poyamba posonkhana inu mu Mpingo, ndimva kuti pakhala malekano mwa inu; ndipo ndivomereza penapo.


pakuti, pokhala pali nkhwidzi ndi ndeu pakati pa inu simuli athupi kodi, ndi kuyendayenda monga mwa munthu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa