Yohane 10:19 - Buku Lopatulika19 Panakhalanso kutsutsana pakati pa Ayuda chifukwa cha mau awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Panakhalanso kutsutsana pakati pa Ayuda chifukwa cha mau awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Anthu adaayambanso kutsutsana okhaokha chifukwa cha mau ameneŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pa mawu awa Ayuda anagawikananso. Onani mutuwo |