Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 1:8 - Buku Lopatulika

8 Iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukachita umboni wa kuunikaku.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukachita umboni wa kuunikaku.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Sikuti iyeyo ndiye anali kuŵalako ai, koma adangobwera kudzachitira umboni kuŵalako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iyeyu sanali kuwunika; koma anabwera ngati mboni ya kuwunika.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 1:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anavomera, wosakana; nalola kuti, Sindine Khristu.


Uku ndiko kuunika kwenikweni, kumene kuunikira anthu onse akulowa m'dziko lapansi.


Inu nokha mundichitira umboni, kuti ndinati, Sindine Khristu, koma kuti ndili wotumidwa m'tsogolo mwake mwa Iye.


Ndipo anati Paulo, Yohane anabatiza ndi ubatizo wa kutembenuka mtima, nati kwa anthu, kuti amkhulupirire Iye amene adzadza pambuyo pake, ndiye Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa