Yohane 1:47 - Buku Lopatulika47 Yesu anaona Natanaele alinkudza kwa Iye, nanena za iye, Onani, Mwisraele ndithu, mwa iye mulibe chinyengo! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Yesu anaona Natanaele alinkudza kwa Iye, nanena za iye, Onani, Mwisraele ndithu, mwa iye mulibe chinyengo! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Pamene Yesu adaona Natanaele akubwera potero, adati, “Mwamuwonatu Mwisraele weniweni wopanda chinyengo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Yesu atamuona Natanieli akuyandikira, anati kwa iye, “Uyu ndi Mwisraeli weniweni, mwa iye mulibe chinyengo.” Onani mutuwo |