Yohane 1:27 - Buku Lopatulika27 ndiye wakudza pambuyo panga, amene sindiyenera kummasulira chingwe cha nsapato yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 ndiye wakudza pambuyo panga, amene sindiyenera kummasulira lamba la nsapato yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Iyeyu ngwobwera pambuyo panga, komabe sindili woyenera ngakhale kumasula zingwe za nsapato zake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iye ndi amene akubwera pambuyo panga, ine siwoyenera kumasula zingwe za nsapato zake.” Onani mutuwo |