Yohane 1:28 - Buku Lopatulika28 Zinthu izi zinachitika mu Betaniya tsidya lija la Yordani, pomwe analikubatiza Yohane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Zinthu izi zinachitika m'Betaniya tsidya lija la Yordani, pomwe analikubatiza Yohane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Zimenezi zidachitikira ku Betaniya, kutsidya kwa mtsinje wa Yordani, kumene Yohane ankabatiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Zonsezi zinachitika ku Betaniya kutsidya lina la mtsinje wa Yorodani, kumene Yohane ankabatizira. Onani mutuwo |