Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 1:2 - Buku Lopatulika

2 Awa anali pachiyambi kwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Awa anali pachiyambi kwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Anali kwa Mulungu chikhalire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mawuwa anali ndi Mulungu pachiyambi.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 1:2
5 Mawu Ofanana  

Pachiyambi Mulungu adalenga kumwamba ndi dziko lapansi.


Ndinali pa mbali pake ngati mmisiri; ndinamsekeretsa tsiku ndi tsiku, ndi kukondwera pamaso pake nthawi zonse;


Ndipo ngati nditi, Sindidzamtchula Iye, sindidzanenanso m'dzina lake, pamenepo m'mtima mwanga muli ngati moto wotentha wotsekedwa m'mafupa anga, ndipo ndalema ndi kupirira, sindingathe kupiriranso.


Pachiyambi panali Mau, ndipo Mau anali kwa Mulungu, ndipo Mau ndiye Mulungu.


Zonse zinalengedwa ndi Iye; ndipo kopanda Iye sikunalengedwe kanthu kalikonse kolengedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa