Yohane 1:1 - Buku Lopatulika1 Pachiyambi panali Mau, ndipo Mau anali kwa Mulungu, ndipo Mau ndiye Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pachiyambi panali Mau, ndipo Mau anali kwa Mulungu, ndipo Mau ndiye Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pachiyambi pa zonse Iye amene amatchedwa dzina loti Mau, anali alipo kale. Anali kwa Mulungu, ndipo anali Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pachiyambi panali Mawu, ndipo Mawu anali kwa Mulungu, ndipo Mawu ndiye Mulungu. Onani mutuwo |