Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:53 - Buku Lopatulika

53 ndipo anakhala chikhalire mu Kachisi, nalikuyamika Mulungu. Amen.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

53 ndipo anakhala chikhalire m'Kachisi, nalikuyamika Mulungu. Amen.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

53 Tsono ankasonkhana m'Nyumba ya Mulungu nthaŵi ndi nthaŵi akutamanda Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

53 Ndipo iwo anakhalabe ku Nyumba ya Mulungu, akulemekeza Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:53
7 Mawu Ofanana  

ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Ndipo iwowa anatuluka, nalalikira ponseponse, ndipo Ambuye anachita nao pamodzi, natsimikiza mau ndi zizindikiro zakutsatapo. Amen.


Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;


Pachiyambi panali Mau, ndipo Mau anali kwa Mulungu, ndipo Mau ndiye Mulungu.


Chisomo cha Ambuye Yesu chikhale ndi oyera mtima onse. Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa